Tag: #Zomba-Thondwe

10
Oct

Zomba-Thondwe Prayer Day

Phungu wa nyumba ya malamulo ku Zomba Thondwe, a Roseby Gadama, wapereka ndalama zokwanira K1 million kwacha kuti ithandize ntchito zampingo. A Gadama ndi mlendo olemekezeka pa mwambo wa mapemphero omwe akuchitika pansi pa utsogoleri wa m’mipingo wa Pastors Fraternal yaku Nasawa, Thondwe, Dzaone ndi Mayaka m’boma la Zomba. Iwo ati achita izi ngati njira imodzi yosangalalira kubadwa kwawo pa

Read more

13
Jun

Hon. Roseby Gadama Brought her Community Together.

When you connect people, magic happens. Sunday 4th of June was a memorable day for the residents of Zomba Thondwe Constituency, who gathered to connect and compete for the 4 million Malawi kwacha trophy sponsored by the area’s Member of Parliament, Hon. Roseby Gadama. Much of our success comes from getting to know people and helping them whenever we can.

Read more